The team at Kodi Fire IPTV strongly suggests that you use a VPN at all times. Be it for browsing, watching Kodi, watching IPTV or anything else – the one that we recommend is Hidden Router. They provide you with very fast speeds, that can reach over 400Mbps, and their VPN service is as low as $6 per month (when paid for 2 years)! Grab your own Hidden Router and regain your online privacy now!
Dont be making politics penapalipose. What is needed is the response not the presence of the the president. We need to save people who are suffering not the presence of the president
Brain ali mkuchikamwa kodi amafuna President wamtundu wanji kweni kweni kunali peter koma nde kunali kumutengetsa lero ndi awa akungolongololave kufusa mafuso azifukwa nthawi zose ngatiiye bdiye olungama nthawi iha anali ku state house anayamba kale kuveka nkhani zakatangale mpaka lero amafuna kuoneka ngati dolo aaaaa uyu mkapolo wamunthu
Malawians have no air planes ✈️ and wherever the president is he can’t leave because he has to use local airports and planes by local routes bwanji atolakhani simutha kufotokozera anthu zenizeni mukufuna kusokoneza dziko ndi nkwiyo osafunikira Brian jonarism yanu mukufuna kuti anthu adzikwiya all the time. We need to encourage people and help people to heal this is a disaster and nobody can’t expect a disaster this is an accident by nature. We are all affected. 😢 we need to respond quickly the same way like the government chidwi chikhale chatonse tiyeni tigwirane manja.
Vuto la ifeyo amalawife sitimaziwa chomwe timafuna ndikhulupilila Kuti achakwera akanatenga ndege ya herokopita ya silikali ija kupita ukuku kukayendera bweziso ena akuyankhula Kuti akungowonongera wonongerabe ndalama Ku south Africa atavuta madzi tsogoleri anayenda pa herokopita komatu kunalibe otukwana
MCP and Tonse Alliance administration they're the same who doesn't care abt Malawian's,,, Nchewa kumwera alibe nako ntchito,,tilibe Presdent kumalawi koma pa 20 March tidzawonetsana theladi…
Mulungu atiyang'anire
Kwa omwe ataya miyoyo yawo mizimu yawo I use muntendere
Akukakamila kwaeni
Koma Pali mafuso enawa mukumafuzila pazifukwatu
Zoonadi brain bomali silili serious kwambili sizitithandizayi
Ngakhare President abwele ndiye kuti Anthu amene amwalirawo awukaso pangofunika chithandizo not zomapanga za President
Dont be making politics penapalipose. What is needed is the response not the presence of the the president. We need to save people who are suffering not the presence of the president
Mr brain musazafe muzangosowa bas
Kodi chilichotse basi president
Chakwera nd mbuzi ya munthu stupid President
Brain akuononga dziko tsiku lina zithu zidzasokonela miss leading amalawi brain
Zopweteka kwambiri Mziko lathu Komanso Ku Mzambique, Madagascar. Ambuye titonthozeni anthu ani akutha
Kodi a chakwerawa malawase sakuwakonda moti akufunitsitsa kuti ndalamaso zomwe akafika zipiteso kwaiyeso iiiiiii
Why is the new minister of information and government spokesman very well respected when he answers the same way as the former one???
The president has dropped the ball. He should have come back the same day the disaster struck.
Zikanakhala kuti palibe malawase ndithudi akanamuuza chilima kuti akamuimile koma poti Pali ndalama aaaaaa ndalama anakoza
Zonsezi chifukwa chokomedwa anzake onse anabwerako iye akutani mpakana lero. Bomali likufunika Bon Kalindo basi.
Mamgunso Brian alibe nzeru kulibe nduna ulibe nzeru imbwa
Imbwa
Braun Ife amalawi tilibe prezdent cakwera mbusa oipa mtima
Galu wa president azake amaiko ena amathamangila kukaina zovuta
A president Zari serious ndi anthu awo. Zikadakala kuti mwana wawo mwamwalira, akanadikira mawa
Brain ali mkuchikamwa kodi amafuna President wamtundu wanji kweni kweni kunali peter koma nde kunali kumutengetsa lero ndi awa akungolongololave kufusa mafuso azifukwa nthawi zose ngatiiye bdiye olungama nthawi iha anali ku state house anayamba kale kuveka nkhani zakatangale mpaka lero amafuna kuoneka ngati dolo aaaaa uyu mkapolo wamunthu
Malawians have no air planes ✈️ and wherever the president is he can’t leave because he has to use local airports and planes by local routes bwanji atolakhani simutha kufotokozera anthu zenizeni mukufuna kusokoneza dziko ndi nkwiyo osafunikira Brian jonarism yanu mukufuna kuti anthu adzikwiya all the time. We need to encourage people and help people to heal this is a disaster and nobody can’t expect a disaster this is an accident by nature. We are all affected. 😢 we need to respond quickly the same way like the government chidwi chikhale chatonse tiyeni tigwirane manja.
Brian Banda machende amako, umati chakwela akwele nde ya umfiti kuti afike msanga?
I think a Brian Banda has natural hatred for the President. Kulankhula ngati khanda munthawi yowawa.
Basi bola ife taziwa kuti tilibe sogoleri wa dziko zikomo Mr brean
Inu president wantundu wanji omangoenda yenda ngati wadya matako agalu osabwera kae bwanji akonze mavutowa
Vuto la ifeyo amalawife sitimaziwa chomwe timafuna ndikhulupilila Kuti achakwera akanatenga ndege ya herokopita ya silikali ija kupita ukuku kukayendera bweziso ena akuyankhula Kuti akungowonongera wonongerabe ndalama Ku south Africa atavuta madzi tsogoleri anayenda pa herokopita komatu kunalibe otukwana
Pule okhuzika wachikondi ndi anthu ake akanasiyiya zonse kuzatsamala zaanthu ake
MCP and Tonse Alliance administration they're the same who doesn't care abt Malawian's,,, Nchewa kumwera alibe nako ntchito,,tilibe Presdent kumalawi koma pa 20 March tidzawonetsana theladi…
Tiyeni tisalozane chala , tingoyan'gana kwa mulungu atichosere vuto li ,,,,,,
Can we conclude kuti apresident alephera kubwelera kukapezeka pa maliro aanthu 66 kaamba koti ndege kulibe?
the worst president in Malawi ndipo atopesa atule pansi udindo
Akuchinda azungu ku america
Ana anjoka inu
Ndaona ine gamlimoto ya Munthu ikutolera maliro gamlimoto olo imodxi ya Boma dzoona
Ndaona ine gamlimoto ya Munthu ikutolera maliro gamlimoto olo imodxi ya Boma dzoona
Kodi achilima mulibe mphamvu yoti kumuudxa chakwera Kuti atsabwerele kumalawi
Brain amayitha
I lost my trust in Chakwera's governance